Laikos Anthu Wamba ndi Utumiki
()
About this ebook
Mawu a Chigiriki akuti LAIKOS akutanthauza “kupanda luso”. Mbiri yatiphunzitsa kwa nthawi ndi nthawi kuti zinthu zazikulu zakwaniritsidwa kudzera kwa anthu amene “anasowekera luso”. Phunzirani, kudzera mu bukhu lapamwambali lolembedwa ndi Dag Heward-Mills, zomwe zimachitika pamene palibe anthu a wamba kugwira ntchito mu tchalitchi; momwe mungagawanirane zolemetsa ndi anthu wamba ndi momwe tikuyenera kulimbanira kuteteza utumiki wa wamba.
Dag Heward-Mills
Bishop Dag Heward-Mills is a medical doctor by profession and the founder of the United Denominations Originating from the Lighthouse Group of Churches (UD-OLGC). The UD-OLGC comprises over three thousand churches pastored by seasoned ministers, groomed and trained in-house. Bishop Dag Heward-Mills oversees this charismatic group of denominations, which operates in over 90 different countries in Africa, Asia, Europe, the Caribbean, Australia, and North and South America. With a ministry spanning over thirty years, Dag Heward-Mills has authored several books with bestsellers including ‘The Art of Leadership’, ‘Loyalty and Disloyalty’, and ‘The Mega Church’. He is considered to be the largest publishing author in Africa, having had his books translated into over 52 languages with more than 40 million copies in print.
Read more from Dag Heward Mills
Those Who Forget Rating: 5 out of 5 stars5/5The Art of Leadership: 3rd Edition Rating: 5 out of 5 stars5/5Church Growth Rating: 5 out of 5 stars5/5Bible Memorisation Handbook Rating: 5 out of 5 stars5/5Ministerial Barrenness Rating: 5 out of 5 stars5/5The Mega Church: 2nd Edition Rating: 5 out of 5 stars5/5Tell Them: 120 Reasons Why You Should Be a Soul Winner Rating: 4 out of 5 stars4/5Model Marriage Rating: 4 out of 5 stars4/51000 Micro Churches Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsWhat it Means to be as Wise as a Serpent Rating: 5 out of 5 stars5/5The Art of Following Rating: 4 out of 5 stars4/5Wisdom Is the Principal Thing for Your Ministry Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsDemons And How To Deal With Them Rating: 5 out of 5 stars5/5The Anointed and His Anointing Rating: 5 out of 5 stars5/5Handbook Of Ceremonies Rating: 4 out of 5 stars4/5Fruitfulness Rating: 5 out of 5 stars5/5Anagkazo - Compelling Power! (2nd Edition) Rating: 5 out of 5 stars5/5
Related to Laikos Anthu Wamba ndi Utumiki
Related ebooks
Laikos: Lay People and the Ministry Rating: 5 out of 5 stars5/5Bible Study for Busy Pastors and Ministers, Volume 2: Ready Made Lessons to Turn Members Into Disciples and an Audience Into an Army Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsAmbiri Aitanidwa Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsReasoning from the Scriptures with Muslims Rating: 4 out of 5 stars4/5The Treasure in the Field: The Treasure in the Field Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsDiscipling Nations: A Workbook on Principles of Discipleship Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsChristlike: The Pursuit of Uncomplicated Obedience Rating: 4 out of 5 stars4/5How Much Is Enough?: Hungering for God in an Affluent Culture Rating: 4 out of 5 stars4/5Escape To A World Of Understanding Antidote to Hatred Against Muslims, Christians and People Everywhere Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsEncounter with God: July–September 2019 Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsEndangered Gospel: How Fixing the World is Killing the Church Rating: 5 out of 5 stars5/5Answering the Call: Saving Innocent Lives One Woman at a Time Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsMoving the Church in 7 STEPs: Strategic, Targeted, Evangelistic, Plans Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsA Collection of Theological Essays Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Atlas of Religion Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsLighthouses: Christian Coaching in a Post-Christian World Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsChurches That Make a Difference: Reaching Your Community with Good News and Good Works Rating: 4 out of 5 stars4/5God’s People Count: Connecting God’s Dots—A Guide through the Book of Numbers Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsWe Cry Justice: Reading the Bible with the Poor People's Campaign Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Hope Habit: How to Confidently Expect God's Goodness in Your Life Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsAdult Bible Studies Fall 2022 Teacher/Commentary Kit Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsA Bishop's Quest: Founding a United Religions Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Domino Effect: Colossians Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsClosing the Floodgates: Setting the Record Straight about Gender and Sexuality Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsUnderstanding the Culture: A Survey of Social Engagement Rating: 4 out of 5 stars4/5Footprints in the African Sand: My Life and Times Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSimply Christian Counselling Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsUnleashed: Stories from All Saints' Booval Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsCrossing the Chasm: A Call to Every Christian to Love Muslim People Rating: 0 out of 5 stars0 ratings
Christianity For You
Boundaries Updated and Expanded Edition: When to Say Yes, How to Say No To Take Control of Your Life Rating: 4 out of 5 stars4/5The 5 Love Languages: The Secret to Love that Lasts Rating: 4 out of 5 stars4/5The Screwtape Letters Rating: 4 out of 5 stars4/5Decluttering at the Speed of Life: Winning Your Never-Ending Battle with Stuff Rating: 4 out of 5 stars4/5Anxious for Nothing: Finding Calm in a Chaotic World Rating: 4 out of 5 stars4/5Present Over Perfect: Leaving Behind Frantic for a Simpler, More Soulful Way of Living Rating: 4 out of 5 stars4/5Changes That Heal: Four Practical Steps to a Happier, Healthier You Rating: 4 out of 5 stars4/5The Story: The Bible as One Continuing Story of God and His People Rating: 4 out of 5 stars4/5The Purpose Driven Life: What on Earth Am I Here For? Rating: 4 out of 5 stars4/5Winning the War in Your Mind: Change Your Thinking, Change Your Life Rating: 5 out of 5 stars5/5Wild at Heart Expanded Edition: Discovering the Secret of a Man's Soul Rating: 4 out of 5 stars4/5Mere Christianity Rating: 4 out of 5 stars4/5The Four Loves Rating: 4 out of 5 stars4/5Less Fret, More Faith: An 11-Week Action Plan to Overcome Anxiety Rating: 4 out of 5 stars4/5Uninvited: Living Loved When You Feel Less Than, Left Out, and Lonely Rating: 4 out of 5 stars4/5A Grief Observed Rating: 4 out of 5 stars4/5The Bible Recap: A One-Year Guide to Reading and Understanding the Entire Bible Rating: 5 out of 5 stars5/5Law of Connection: Lesson 10 from The 21 Irrefutable Laws of Leadership Rating: 4 out of 5 stars4/5Good Boundaries and Goodbyes: Loving Others Without Losing the Best of Who You Are Rating: 5 out of 5 stars5/5The 21 Irrefutable Laws of Leadership: Follow Them and People Will Follow You Rating: 4 out of 5 stars4/5NIV, Holy Bible Rating: 4 out of 5 stars4/5The Book of Enoch Rating: 4 out of 5 stars4/5Everybody, Always: Becoming Love in a World Full of Setbacks and Difficult People Rating: 4 out of 5 stars4/5Don't Give the Enemy a Seat at Your Table: It's Time to Win the Battle of Your Mind... Rating: 5 out of 5 stars5/5Boundaries Workbook: When to Say Yes, How to Say No to Take Control of Your Life Rating: 4 out of 5 stars4/5Girl, Wash Your Face: Stop Believing the Lies About Who You Are so You Can Become Who You Were Meant to Be Rating: 3 out of 5 stars3/5The Holy Bible (World English Bible, Easy Navigation) Rating: 4 out of 5 stars4/5I Guess I Haven't Learned That Yet: Discovering New Ways of Living When the Old Ways Stop Working Rating: 4 out of 5 stars4/5
Reviews for Laikos Anthu Wamba ndi Utumiki
0 ratings0 reviews
Book preview
Laikos Anthu Wamba ndi Utumiki - Dag Heward-Mills
LAIKOS
Anthu Wamba ndi Utumiki
Anthu wamba
Abusa Wamba
Odzipereka
DAG HEWARD-MILLS
Kupatula ngati kutchulidwa kwina, Malemba onse achokera mu Baibulo la Bukhu Lopatulika La Chichewa 1966
Umwini © 2019 Dag Heward-Mills
Kutsindikiza koyamba 2019 ndi Parchment House
Dziwani zambiri zokhudza Dag Heward-Mills pa:
Healing Jesus Campaign
Lemberani kwa: evangelist@daghewardmills.org
Webusaiti: www.daghewardmills.org
Facebook: Dag Heward-Mills
Twitter: @EvangelistDag
ISBN: 978-1-64329-025-6
Umwini wonse wasungidwa pansi pa lamulo la umwini lapadziko. chilolezo cholembedwa chikuyenera kutengedwa kuchokera kwa wosindikiza kuti mugwiritse ntchito kapena kutulutsa kachikena gawo lili lonse la bukhu limeli, pokha pokha mawu ochepa mu maganizo ofunikira kwambiri kapena nkhani.
Zamkatimu
Mutu 1: LAIKOS: Munthu Wamba
Mutu 2: Zomwe Zimachitika Ngati Palibe Anthu Wamba ndi Odzipereka
Mutu 3: Zifukwa Zisanu ndi Ziwiri Zomwe Mulungu Amagwirira Ntchito Kudzera Mwa Anthu Wamba
Mutu 4: Zinthu Zisanu ndi Ziwiri Muyenera Kudziwa Zokhudza Utumiki wa Wamba
Mutu 5: Zifukwa Zhomwe Mukuyenera Kukhalira M’busa Wamba
Mutu 6: Momwe Ndinagwirira Ngati M’busa Wamba
Mutu 7: Mmene Mungagawirane Kulemedwa ndi Anthu Wamba
Mutu 8: M’busa Wamba Wabwino
Mutu 9: Kodi Khalidwe Labwino la M’busa Wamba ndi Lotani?
Mutu 10: Abusa Wamba a Mitima Iwiri
Mutu 11: Kumvetsetsa Momwe Utumiki wa Wamba Uliri Muyezo wa Utumiki
Mutu 12: Kumvetsetsa Momwe Utumiki wa Wamba Uliri Mtundu wa Utumiki Wothandiza
Mutu 13: Kumvetsetsa Zosowekera mu Utumiki wa Wamba
Mutu 14: Kumvesetsa Zifukwa Zimene Mulungu Amalolera Utumiki Wa Wamba Kukhalapo
Mutu 15: Kuzani Maluso Anayi Ofunika a M’busa Wamba
Mutu 16: Mabvuto a Abusa a Wamba
Mutu 17: Utumiki Wokhazikitsa Chitsanzo wa Odzipereka
Mutu 18: Chifukwa Chomwe Tikuyenera Kulimbana Kuteteza Utumiki wa Wamba
Mutu 1
LAIKOS: Munthu Wamba
Mawu oti munthu wamba adachokera ku mawu a chigiliki oti LAIKOS amane amatanthauza kuti munthu wopanda upangiri
. Mbri imatiphunzitsa kuti zinthu zazikulu zikhoza kuchitika kudzera mwa anthu opanda upangiriwa. Kuchita machawi ndikuyang’anitsitsa anthu wamba, kudzakulimbikitsani ndipo mudzawagwiritsa ntchito mu utumiki. Kudzera mwa anthu wamba, miyoyo ya anthu idzapulumuka, milaga idzakhazikika, mipingo idzakula ndipo ntchito ya Mulungu idzayenda bwino.
Awa ndi matanthauzo ochepa a mawu oti munthu wamba:
1. Munthu wamba ndi munthu wopanda upangiri.
2. Munthu wamba ndi munthu wabwinobwino.
3. Munthu wamba ndi munthu wa ponseponse.
4. Munthu wamba ndi munthu wachizolowezi.
5. Munthu wamba ndi munthu wokhazikika.
6. Munthu wamba ndi munthu wa chabe chabe
7. Munthu wamba ndi munthu watsiku lililonse.
8. Munthu wamba ndi munthu wapafupipafupi
9. Munthu wamba si katswiri.
10. Munthu wamba ndi munthu amene alibe ukadaulo uliwonse.
11. Munthu wamba ndi munthu amene siwapaderadera.
12. Munthu wamba ndi munthu amene alibe luso la mtundu uliwonse.
13. Munthu wamba ndi amene sadaphunzitsidwe.
14. Munthu wanba ndi amene alibe zomuyenereza kapena mbiri yabwino.
15. Munthu wamba ndi munthu amene alibe chilolezo
Zokwaniritsa Zikuluzikulu mu Mpingo pa Dziko Lonse
1. Anthu wamba adali nsanamira wa zochitika zosintha tchalitchi.
Kumasulira kwa baibulo ndi Martin Luther muchiyankhu cha munthu wamba zinasintha dziko lonse. M’malo mongokhala muchilatini, Baibulo lidakhala lowerengeka ndi munthu wamba. Pamene anthu wamba adakhla ndi chivumbulutsa cha chidziwitso, iwo adasintha dziko. Kuzindikira kuti chipulumutso chidali chaulere kwa munthu aliyense kudzera mu chisomo cha Mulungu iwo adadzidzimuka ndi kulimbikitsa kukonzanso kwazinthu.
2. Anthu wamba ndiye adali nsanamira za mpingo waukulu wa Methodisti
M’zaka zambiri za m’mbuyomu, chipembedzo cha chimethodisti chinali chipembedzo cha chikulu cha chiprotestanti ku Amerika. Chipembedzochi cha yendetsedwa ndi mphamvu za anthu wamba.
Chikhalidwe cha kale cholalikira mu mipingo ya chimthodisiti chidali choti olalika wa wamba amasankhidwa kutsogolera mpingo ndi kulalikira m’magulu otchedwa dera
Olalika wamambayu amayenda kapena kukwera pa kavalo, m’dera loyikika kukalalika molinga ndi ndondomeko ndi nthawi yoikidwayo.
Ngakhale padali kusankha abusa ndi atumiki, kulalikira kudzera mwa anthu wambaku kudapititirabe ndi alaliki a chipemebedzo cha chimethodisiti. Iwowa amasankhidwa ndi mipingo yosisiyanasisyana kudzalalika mmalo mwa mlaliki wina amene wachokapo.
3. Anthu wamba adali nsanamira za mpingo umodzi waukulu padziko lonse lapansi.
Imodzi mwa mfundo zikulu zikulu imene mpingo wa Yoido udamangidwapo, ndiyakugwira ntchito kudzera mwa anthu wamba.
Mpingo waYoido udayambitsi ndi Davide Yonggi Cho ndipo apongozi ake a Choi Ja-shil, onse amene adali abusa Asembulesi, adali ndi mapemphero a dera pa 15 Meyi, 1958 ndi amayi ena anayi kunyumba kwa Choi Ja-shil.
Umembala wa tchalichi udafika zikwi zisanu mu chaka cha 1977, namabalayi idawiriza mu zaka ziwiri zosatsatizo. Pa 30 Novembala 1981 nambala ya anthu idakwera kukafika pa zikwi 200. Pa nthawi imeneyi, uwu udali mpingo waukulu pa dziko lonse ndipo udadziwika ndi nyuzi pepa ya Los Angeles.
Mu chaka cha 2007, tchalitchi chinali ndi mamembala okwana 830,000 ndi mikumano isanu ndi ziwiri lamulungu lokha muziyankhulo zokwana khumi chisanu ndi chimodzi.
4. Anthu wamba ndi msanamira za mgwirizano waukulu Wa mipingo yochokera Ku Nigeria ndi Ku Ghana.
Tchalichi cha Redeemed chaku Nigeria ndi tchalichi cha Pentekositi chimene likulu lake liri ku Ghana imadziwika ndi kugwiritsa ntchito bwino anthu wamba. Onse mwa matchalitchi amenewa ali ndi mgwirizano waukulu wa mipingo ndipo amagwiritsa ntchito anthu wamba kulalika ndi ubusa.
Tchalichi cha pentekositi chidayambitsidwa ndi James Mckeon, m’ mishonale wotumizidwa ndi tchalichi cha Apositoli cha Ku Bradford, UK kupita ku Gold Coast.
Chidakula nkukhala ndi ma membala okwana 1.7 miliyoni. Tchalitchi cha Pentekositi chili ndi mipingo yokwana zikwi khumi ndi zitatu mmaiko okwana makumi asanu ndi awiri pa dziko lonse.
Mu chaka cha 1952, Pa Josiah Akindayomi adayanbitsa mipingo wa Redeemed ku Nigeria.
Pansi pa ulamuliro wa woyang’anira wa mipingo yonse, M’busa E.A Adeboye mpingowu wakula kufikira mmaiko oposa zana limodzi ndi makumi anayi ndi ma miliyoni a mamembala.
Zoonadi uku nkukwaniritsa zazikulu ndithu ndipo izi zidatheka chifukwa chogwiritsa ntchito anthu wamba.
Zokwaniritsa Zazikulu mu Dziko la Chikunja
1. Boma la demokalase lidayambidwa ndi anthu wamba
Demokalase ndikupereka mwayi ofanana kwa anthu kuti achitepo kanthu ndi kusintha boma lawo ngati akufuna.
Demokalase ndi mphamvu ya anthu wamba kukana kukhala nyengo zimene sakukondwera nazo.
Demokalase nkutengapo mbali kwa anthu wamba ndikuchitsa zinthu kusintha mu dziko.
Demokalase idamangidwa pa mfundo yopereka mwayi ofanana kwa anthu wamba.
2. Dziko lamphamvu yaikulu lidayamba chifukwa cha anthu wamba.
Kusintha kwa Amerika ndi chitsanzo