Kupeza Kudzoza
()
About this ebook
Kudzoza ndi chifungulo chachichikulu chofunikira kutsegula khomo la kuchita bwino ndo kukwaniritsa utumiki. Anthu ambiri ayesera kuchita ntchito ya Mulungu chifukwa cha mafuno abwino, popanda kufika kutali analephera kuzindikira kuti “Ndi khamu la nkhondo ai, ndi mphamvu ai, koma ndi Mzimu Wanga (Kudzoza)” [Zekariya 4:4].
Bukhu lapderali “Kupeza Kudzoza” lolembedwa ndi Bishopu Dag Heward-mills lizakuphunzitsani inu zomwe zimatanthauza kupeza kudzoza ndi momwe mungapangire! Lolani chikhumbo khumbo cha Kudzoza kwa Mulungu kutakasike mkati mwanu kudzera mu masamba a m’bukhuli!
Dag Heward-Mills
Bishop Dag Heward-Mills is a medical doctor by profession and the founder of the United Denominations Originating from the Lighthouse Group of Churches (UD-OLGC). The UD-OLGC comprises over three thousand churches pastored by seasoned ministers, groomed and trained in-house. Bishop Dag Heward-Mills oversees this charismatic group of denominations, which operates in over 90 different countries in Africa, Asia, Europe, the Caribbean, Australia, and North and South America. With a ministry spanning over thirty years, Dag Heward-Mills has authored several books with bestsellers including ‘The Art of Leadership’, ‘Loyalty and Disloyalty’, and ‘The Mega Church’. He is considered to be the largest publishing author in Africa, having had his books translated into over 52 languages with more than 40 million copies in print.
Read more from Dag Heward Mills
Bible Memorisation Handbook Rating: 5 out of 5 stars5/5The Art of Leadership: 3rd Edition Rating: 5 out of 5 stars5/5Those Who Forget Rating: 5 out of 5 stars5/5The Mega Church: 2nd Edition Rating: 5 out of 5 stars5/5Ministerial Barrenness Rating: 5 out of 5 stars5/5Wisdom Is the Principal Thing for Your Ministry Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsTell Them: 120 Reasons Why You Should Be a Soul Winner Rating: 4 out of 5 stars4/5What it Means to be as Wise as a Serpent Rating: 5 out of 5 stars5/5Model Marriage Rating: 4 out of 5 stars4/5Church Growth Rating: 5 out of 5 stars5/51000 Micro Churches Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Art of Following Rating: 4 out of 5 stars4/5Flow Prayer Book Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsFruitfulness Rating: 5 out of 5 stars5/5The Anointed and His Anointing Rating: 5 out of 5 stars5/5Demons And How To Deal With Them Rating: 5 out of 5 stars5/5Handbook Of Ceremonies Rating: 4 out of 5 stars4/5Anagkazo - Compelling Power! (2nd Edition) Rating: 5 out of 5 stars5/5
Related to Kupeza Kudzoza
Related ebooks
Catch the Anointing Rating: 5 out of 5 stars5/5Say What?: A Biblical and Historical Journey on the Connection between the Holy Spirit, Prophecy, and Tongues Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsKnowledge Revealed: Discover Hidden Secrets in the Bible for Those Who Want to Know More Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Mystery of Life Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsRivers and Wells Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsRevelation: Putting the Cookies on the Bottom Shelf Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsYou Are Wonderful: A Devotional Insight into the Names and Descriptions of God and Jesus in the Bible Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsNew Order of Worship Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsOn the Great Reunion Ingathering Journey: A Study for the Journey Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Anchor Leg: Restoring First-Century Holiness and Power Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsChrist Second Coming, a Message for the Church: The Mysteries of Spirits and Their Roles in Prophecy Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSurprised by the Holy Spirit Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsConforming to God’s Standard: The Basis for a Successful Christian Living Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSubdued Memories Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsAccessing the Scriptures: The King Is Coming Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Great Commission Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsLearning to Heal: A Pratical Guide for Every Christian Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Baptism of Fire, Personal Revival, Renewal and the Anointing for Supernatural Living Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsHell No: The Surprising Truths the Bible Teaches about Death, Resurrection, and Judgment Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSeven Steps to Have a Devotion Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsAn In-depth Study of The Holy Spirit of Promise Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsTaking Action: Receiving and Operating in the Gifts and Power of the Holy Spirit Rating: 4 out of 5 stars4/5Unveiling the End Times in Our Time: The Triumph of the Lamb in Revelation Rating: 5 out of 5 stars5/5Walk This Way: The Spirit-Led Life Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Infilling of the Holy Spirit: Christ's (His) Discipline for Kingdom Living Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsI AM JESUS: Understanding Jesus Through His “I Am” Proclamations Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsChrist Is the End of the Law: The 21st Century Epistle Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsImmersion Bible Studies: John Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsBible Overview Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsMansions of the Heart: Exploring the Seven Stages of Spiritual Growth Rating: 4 out of 5 stars4/5
Christianity For You
Boundaries Updated and Expanded Edition: When to Say Yes, How to Say No To Take Control of Your Life Rating: 4 out of 5 stars4/5Mere Christianity Rating: 4 out of 5 stars4/5Decluttering at the Speed of Life: Winning Your Never-Ending Battle with Stuff Rating: 4 out of 5 stars4/5The 5 Love Languages: The Secret to Love that Lasts Rating: 4 out of 5 stars4/5The Screwtape Letters Rating: 4 out of 5 stars4/5Law of Connection: Lesson 10 from The 21 Irrefutable Laws of Leadership Rating: 4 out of 5 stars4/5Anxious for Nothing: Finding Calm in a Chaotic World Rating: 4 out of 5 stars4/5Winning the War in Your Mind: Change Your Thinking, Change Your Life Rating: 5 out of 5 stars5/5The Purpose Driven Life: What on Earth Am I Here For? Rating: 4 out of 5 stars4/5Uninvited: Living Loved When You Feel Less Than, Left Out, and Lonely Rating: 4 out of 5 stars4/5Good Boundaries and Goodbyes: Loving Others Without Losing the Best of Who You Are Rating: 5 out of 5 stars5/5Girl, Wash Your Face: Stop Believing the Lies About Who You Are so You Can Become Who You Were Meant to Be Rating: 3 out of 5 stars3/5Wild at Heart Expanded Edition: Discovering the Secret of a Man's Soul Rating: 4 out of 5 stars4/5The 21 Irrefutable Laws of Leadership: Follow Them and People Will Follow You Rating: 4 out of 5 stars4/5The Four Loves Rating: 4 out of 5 stars4/5Changes That Heal: Four Practical Steps to a Happier, Healthier You Rating: 4 out of 5 stars4/5The Stories We Tell: Every Piece of Your Story Matters Rating: 3 out of 5 stars3/5Present Over Perfect: Leaving Behind Frantic for a Simpler, More Soulful Way of Living Rating: 4 out of 5 stars4/5A Grief Observed Rating: 4 out of 5 stars4/5The Book of Enoch Rating: 4 out of 5 stars4/5Less Fret, More Faith: An 11-Week Action Plan to Overcome Anxiety Rating: 4 out of 5 stars4/5How to Lead When You're Not in Charge: Leveraging Influence When You Lack Authority Rating: 4 out of 5 stars4/5I'll Start Again Monday: Break the Cycle of Unhealthy Eating Habits with Lasting Spiritual Satisfaction Rating: 4 out of 5 stars4/5NIV, Holy Bible Rating: 4 out of 5 stars4/5The Bible Recap: A One-Year Guide to Reading and Understanding the Entire Bible Rating: 5 out of 5 stars5/5The Magnolia Story (with Bonus Content) Rating: 4 out of 5 stars4/5Everybody, Always: Becoming Love in a World Full of Setbacks and Difficult People Rating: 4 out of 5 stars4/5Boundaries Workbook: When to Say Yes, How to Say No to Take Control of Your Life Rating: 4 out of 5 stars4/5
Reviews for Kupeza Kudzoza
0 ratings0 reviews
Book preview
Kupeza Kudzoza - Dag Heward-Mills
Kupeza
Kudzoza
DAG HEWARD-MILLS
Parchment House
Kupatula ngati kutchulidwa kwina, Malemba onse achokera mu Baibulo la Bukhu Lopatulika La Chichewa 1966
Mutu Woyambirira: Catch the Anointing
Mawu otengedwa kuchokera mu A Passion For The Gospel (Chilakolako Cha Uthenga Wabwino) ndi Colin Whittaker. Kugwiritsidwa ntchito ndi chilolezo cha Kingsway Publications, Lathbridge Drove, Eastbourne, BN23 6NT
Mawu otengedwa kuchokera mu Understanding the Anointing (Kumvetsetsa Kudzoza) ndi Kenneth Hagin. Kugwiritsidwa ntchito ndi chilolezo cha Faith Library Publications & Kenneth Hagin Ministries Inc.
Mawu otengedwa kuchokera mu All Things are Possible (Zonse ndi Zotheka) ndi David Edwin Harrel Jnr. Kugwiritsidwa ntchito ndi chilolezo cha Indiana University Press
Mawu otengedwa kuchokera mu The Release of Power (Kumasulidwa kwa Mphamvu) ndi Bishop David A. Oyedepo. Kugwiritsidwa ntchito ndi chilolezo cha Dominion Publishing House
Mawu otengedwa kuchokera mu Tragedy Trauma Triumph - WHY? (Tsoka Kupyeteka Chipambano-CHIFUKWA?) ndi T.L. Osborne.Kugwiritsidwa ntchito ndi chilolezo cha OSFO International
Umwini © 2019 Dag Heward-Mills
Kutsindikiza ndi Parchment House 2019
Kutsindikiza koyamba ndi Parchment House 2019
ISBN:
Dziwani zambiri zokhudza Dag Heward-Mills pa:
Healing Jesus Campain
Lemberani kwa: evangelist@daghewardmills.org
Webusaiti: www.daghewardmills.org
Facebook: Dag Heward-Mills
Twitter: @EvangelistDag
Kuperekedwa
Ndikulipereka bukhu ili kwa Bishopu Nicholas Duncan-Williams.
Zikomo chifukwa chopangira njira mpingo ku Ghana.
Umwini wonse wasungidwa pansi pa umwini lamulo la umwini lapadziko. chilolezo cholembedwa chikuyenera kutengedwa kuchokera kwa wosindikiza kuti mugwiritse ntchito kapena kutulutsa kachikena gawo lili lonse la bukhu limeli, pokha pokha mawu ochepa mu maganizo ofunikira kwambiri kapena nkhani
Zamkatimu
Mutu 1: Muyenera Kukhala Odzozedwa
Mutu 2: Kulumikizana ndi Anthu a Mulungu
Mutu 3: Luso la Kumvetsera Matepi
Mutu 4: Umboni Wanga
Mutu 5: Pezani Kudzodza
Mutu 6: Luso la Kulalikira ndi Kudzoza
Mutu 7: Aman
ndi Tsalach
Mutu 8: Zimphona Zisanu ndi Chimodzi Zimagwira Kudzoza
Mutu 9: Chifukwa Chimene Anthu Ena Sapezera Kudzoza
Mutu 1
Muyenera Kukhala Odzozedwa
Ndinalibe maphunziro apadera mu utumiki; sindinapite ku sukulu ya Baibulo ndinso kucheza kochepa kwambiri ndi anthu aakulu a Mulungu. Pamene ndinayamba kulowa mu utumiki, ena mwa anthu a Mulungu amene ndinalumikizana nawo, anayamba kukayikira kuitana kwa Mulungu pa moyo wanga. Ndinalibe njira koma ndikugwiritsira ntchito kudzoza komwe kunali pa anthu ena Mulungu akutali kudzera mu matepi ndi mabuku awo.
Ine ndikukhulupirira kuti ine ndiri wodzozedwa ndi Mzimu Woyera kuti ndiime mu ofesi yanga ya utumiki. Ndili ndi umboni wochuluka wozungulira ine kuti ndikayike za kudzoza pamoyo wanga. Ndikukhulupiliranso kuti chitukuko cha tekinoloje ndi zamakono pa dziko lapansi ndi cholinga chakuthandizira ufumu wa Mulungu ndi utumiki. Tekinoloje yatithandizira kukhala pafupi ndi anthu odzozedwa.
Ndiko kudzoza kumene mumasowekera
Pamene Mulungu akutumizirani munthu wa Mulungu, mumapatsidwa mpata wolandira iye ndikugwira kudzoza komwe kuli pa moyo wake. Kudzoza ndi chinthu chachikulu chomwe iwe ndi ine tikufunikira kuchita ntchito ya Mulungu. Mneneri Zakariya ankadziwa kuti chinthu chofunika kwambiri chinali kudzoza. Ndi khamu la ankhondo ai, ndi Mphamvu ai, koma ndi Mzimu wanga
(Zekariya 4: 6).
Elisa anazindikiranso kuti chinthu chimene chinapangitsa utumiki wa Eliya kukhala wopambana chinali kudzoza. Pamene iye anali nawo mwayi, iye anapempha kudzoza. Anthu ena ayenera kuti anapempha ndalama, maphunziro kapena ziyeneretso zomwe Eliya anali nazo. Koma Elisha ankafuna kudzoza!
Ndipo kunali ataoloka, Eliya adati kwa Elisa, tapempha chimene ndikuchitire, ndisanachotsedwe kwa iwe. Ndipo Elisa anati, mundipatse magawo awiri a mzimu wanu akhale pa ine.
2 Mafumu 2: 9
Mu bukhu ili, ndikufuna kugawana nanu za njira yodzoza yomwe siyinenedwa kawirikawiri. Zingamveke zatsopano kwa inu, koma zenizeni. Ngati pali njira iliyonse yomwe mungapezere kudzoza, chonde tengani! Ine sindikupereka ichi monga njira yokha yomwe Mulungu angakudzozereni inu; Ndikugawana nanu zomwe ndalandira kuchokera kwa Ambuye. Ndikugawana nanu zomwe zili m’Baibulo komanso zomveka bwino.
Anthu ambiri adzalandira kudzoza mwa kumvetsera matepi ndi kuwerenga mabuku, koma samvetsa zomwe zawachitikira. Ambiri mwa iwo omwe adalandira kudzoza kudzera mu njirayi sangathe kuphunzitsa chifukwa sakuwamvetsa bwino. Ndikukhulupirira kuti ndi ntchito yanga kuphunzitsa njira yosavuta komanso yeniyeni yogwirira chofunikira kwambiri pa utumiki - kudzoza.
Mutu 2
Kulumikizana ndi Anthu a Mulungu
Bukhu lina, ndagawana nanu za kufunikira kolumikizana ndi munthu wa Mulungu kuti mudzalandire kudzoza kumene kuli pamoyo wake. N’chifukwa chiyani muyenera kulumikizana ndi