Zoopsa Zauzimu
()
About this ebook
Mkhristu amayenda mkati kati mwa zoopsa zambiri ndi misampha. Bukhuli likatsekula maso anu ku zoopsa zambiri zobisika zomwe zikudikira kukupwetekani, kuvulaza komanso kuononga. Dzithandizeni nokha, dzipulumutseni nokha kudzera mu bukhu lamphamvu ili la zoopsa zauzimu!
Dag Heward-Mills
Bishop Dag Heward-Mills is a medical doctor by profession and the founder of the United Denominations Originating from the Lighthouse Group of Churches (UD-OLGC). The UD-OLGC comprises over three thousand churches pastored by seasoned ministers, groomed and trained in-house. Bishop Dag Heward-Mills oversees this charismatic group of denominations, which operates in over 90 different countries in Africa, Asia, Europe, the Caribbean, Australia, and North and South America. With a ministry spanning over thirty years, Dag Heward-Mills has authored several books with bestsellers including ‘The Art of Leadership’, ‘Loyalty and Disloyalty’, and ‘The Mega Church’. He is considered to be the largest publishing author in Africa, having had his books translated into over 52 languages with more than 40 million copies in print.
Read more from Dag Heward Mills
The Art of Following Rating: 4 out of 5 stars4/5Those Who Forget Rating: 5 out of 5 stars5/5Bible Memorisation Handbook Rating: 5 out of 5 stars5/5Ministerial Barrenness Rating: 5 out of 5 stars5/5The Art of Leadership: 3rd Edition Rating: 5 out of 5 stars5/5Church Growth Rating: 5 out of 5 stars5/5The Mega Church: 2nd Edition Rating: 5 out of 5 stars5/5Tell Them: 120 Reasons Why You Should Be a Soul Winner Rating: 4 out of 5 stars4/5Wisdom Is the Principal Thing for Your Ministry Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsModel Marriage Rating: 4 out of 5 stars4/51000 Micro Churches Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsWhat it Means to be as Wise as a Serpent Rating: 5 out of 5 stars5/5Demons And How To Deal With Them Rating: 5 out of 5 stars5/5Fruitfulness Rating: 5 out of 5 stars5/5The Anointed and His Anointing Rating: 5 out of 5 stars5/5Handbook Of Ceremonies Rating: 4 out of 5 stars4/5Anagkazo - Compelling Power! (2nd Edition) Rating: 5 out of 5 stars5/5Flow Prayer Book Rating: 0 out of 5 stars0 ratings
Related to Zoopsa Zauzimu
Related ebooks
Spiritual Dangers Rating: 4 out of 5 stars4/5Man Up Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsGolden Nuggets From God's Word Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSupernatural Living Rating: 5 out of 5 stars5/5God's Guidebook to Business...as Taught by an Angel Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSeeking God for Daily Living and Destiny Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsJust a Little Bit More Faith: How to Walk and not Faint Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsClose Encounters with Christ: The Vision Dwells Within Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Great Definer Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsHow God Does Miracles Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsRestoring Order in a Chaotic World Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsThe Blameless Body Routine: Exercise your Faith in Spirit, Soul and Body Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsBorn For A Purpose Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsJudgment: The Boomerang Effect Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsSTORIES FROM THE TRAIL: Finding God in Everyday Life Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsFrom His Lips: On Our Vision: From His Lips, #3 Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsIn His Image, in His Likeness Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsCompleteness in Christ Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsENERGY DRINK : CALORIES: WISDOM Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsChristianity from the Eyes of a Child: Creation’s History from the Bible; Science Had It Right All Along Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsBeyond the Scriptures Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsLiving Your Created Design: A Pep Talk for Your Journey Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsRising to Your Next Level: Biblical Principles for Your Desired Destiny Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsDoes Money Answer All Things? Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsLost Wonder: Power from the Writings of Luke Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsRideshare Adventures in Evangelism Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsLiving with the Mind of a Reprobate Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsHow To Live A Perfect Life In Christ Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsServing up God: My Workplace as a Ministry Rating: 0 out of 5 stars0 ratingsMaking Spiritual Progress (Volume 2): Making Spiritual Progress, #8 Rating: 0 out of 5 stars0 ratings
Christianity For You
The Book of Enoch Rating: 4 out of 5 stars4/5Winning the War in Your Mind: Change Your Thinking, Change Your Life Rating: 5 out of 5 stars5/5Mere Christianity Rating: 4 out of 5 stars4/5Anxious for Nothing: Finding Calm in a Chaotic World Rating: 4 out of 5 stars4/5The Story: The Bible as One Continuing Story of God and His People Rating: 4 out of 5 stars4/5The 5 Love Languages: The Secret to Love that Lasts Rating: 4 out of 5 stars4/5The Purpose Driven Life: What on Earth Am I Here For? Rating: 4 out of 5 stars4/5The Holy Bible (World English Bible, Easy Navigation) Rating: 4 out of 5 stars4/5Unoffendable: How Just One Change Can Make All of Life Better (updated with two new chapters) Rating: 5 out of 5 stars5/5The 21 Irrefutable Laws of Leadership: Follow Them and People Will Follow You Rating: 4 out of 5 stars4/5The Bible Recap: A One-Year Guide to Reading and Understanding the Entire Bible Rating: 5 out of 5 stars5/5Girl, Wash Your Face: Stop Believing the Lies About Who You Are so You Can Become Who You Were Meant to Be Rating: 3 out of 5 stars3/5Boundaries Updated and Expanded Edition: When to Say Yes, How to Say No To Take Control of Your Life Rating: 4 out of 5 stars4/5Boundaries Workbook: When to Say Yes, How to Say No to Take Control of Your Life Rating: 4 out of 5 stars4/5The Good Girl's Guide to Great Sex: Creating a Marriage That's Both Holy and Hot Rating: 4 out of 5 stars4/5Uninvited: Living Loved When You Feel Less Than, Left Out, and Lonely Rating: 4 out of 5 stars4/5The Screwtape Letters Rating: 4 out of 5 stars4/5Changes That Heal: Four Practical Steps to a Happier, Healthier You Rating: 4 out of 5 stars4/5The Unseen Realm: Recovering the Supernatural Worldview of the Bible Rating: 5 out of 5 stars5/5Winning the War in Your Mind Workbook: Change Your Thinking, Change Your Life Rating: 5 out of 5 stars5/5Present Over Perfect: Leaving Behind Frantic for a Simpler, More Soulful Way of Living Rating: 4 out of 5 stars4/5Decluttering at the Speed of Life: Winning Your Never-Ending Battle with Stuff Rating: 4 out of 5 stars4/5Your Brain's Not Broken: Strategies for Navigating Your Emotions and Life with ADHD Rating: 5 out of 5 stars5/5Wild at Heart Expanded Edition: Discovering the Secret of a Man's Soul Rating: 4 out of 5 stars4/5The Four Loves Rating: 4 out of 5 stars4/5How to Lead When You're Not in Charge: Leveraging Influence When You Lack Authority Rating: 4 out of 5 stars4/5I'll Start Again Monday: Break the Cycle of Unhealthy Eating Habits with Lasting Spiritual Satisfaction Rating: 4 out of 5 stars4/5
Reviews for Zoopsa Zauzimu
0 ratings0 reviews
Book preview
Zoopsa Zauzimu - Dag Heward-Mills
Zoopsa Zauzimu
DAG HEWARD-MILLS
Kupatula ngati kutchulidwa kwina, Malemba onse achokera mu Baibulo la Bukhu Lopatulika La Chichewa 1966
Mutu Woyambirira: Spiritual Dangers
Umwini © 2019 Dag Heward-Mills
Kutsindikiza koyamba 2019 ndi Parchment House
Dziwani zambiri zokhudza Dag Heward-Mills pa:
Healing Jesus Campaign
Lemberani kwa: evangelist@daghewardmills.org
Webusaiti: www.daghewardmills.org
Facebook: Dag Heward-Mills
Twitter: @EvangelistDag
ISBN: 978-1-64135-966-5
Umwini wonse wasungidwa pansi pa lamulo la umwini lapadziko. chilolezo cholembedwa chikuyenera kutengedwa kuchokera kwa wosindikiza kuti mugwiritse ntchito kapena kutulutsa kachikena gawo lili lonse la bukhu limeli, pokha pokha mawu ochepa mu maganizo ofunikira kwambiri kapena nkhani
Zamkatimu
Mutu 1: Chifukwa Chani Zinthu Zina Ziyenera Kuchitidwa Moyambirila
Mutu 2: Chifukwa Chomwe Ufumu wa Mulungu Ukuyenera Kukhalira Chokonda Chanu Choyamba
Mutu 3: Kuopsa kwa Dama
Mutu 4: Ndondomeko Zopewera Dama
Mutu 5: Zifungulo za Uzimu Zopewera Dama
Mutu 6: Kodi Mkazi Wachiwerewere Ndi Ndani?
Mutu 7: Zizindikiro za Mkazi Wachiwerewere
Mutu 8: Mkazi wachiwerewere mu Baibulo
Mutu 9: Zifunguro Khumi Zotithandiza Kumvetsetsa Zikhumbokhumbo Athu pa Akazi
Mutu 10: Kuopsya Kokhala Moyo wa Pawiri
Mutu 11: Mitundu Khumi ya moyo wapawiri
Mutu 1
Chifukwa Chani Zinthu Zina Ziyenera Kuchitidwa Moyambirila
Zisankho za zinthu zolakwikwa ndi zinthu zoopsa kwa Akhristu. Ukakhala munthu wochimwa, umangosankha pakati pa zinthu ziwiwri: zabwino ndi zoipa. Pamene ukukula mwa Ambuye, zisankho zanu zimakhala zochuluka, ndipo mumakhala ndi zambiri zakuti musankhepo.
Nthawi imeneyi zisankho zanu sizimakhalanso za pakati pa zoipa ndi zabwino koma pakati pa zabwino ndi zabwino. Kutengera pa zimene mukufuna kukachita, pamakhala kawiri kawiri zinthu zochuluka zabwino zakuti mukasankhepo. Pamene mwafika pa malo amenewo kumakhala kofunikila kuti mukazindikile mfundo iyi ya dongosolo la zisankho: Ndi chiti chimene ndichite moyambirila?
Yesu adatipatsa vumbulutso lalikulu pa zinthu zina zomwe zikuyenera kuchitidwa zina zisanachitidwe.
Ndizosangalatsa kukasanthula kuchuluka kwake kwa zinthu zimene Yesu adanena kuti zikuyenera kukachitidwa moyambirila. Pena paliponse pamene Yesu ankalankhula za zinthu zoyambilila kwambiri, adagwiritsa ntchito liwu la chi Greek lakuti proton. Mu bukhu limeneli tikuyang’na pa zinthu za proton; zinthu zomwe Yesu adanena zichitidwe moyambirila.
Monga M’khristu, mukuyenera kukchita zinthu zoyambirila moyambirila. Zinthu zoyambirila moyambirila zikutanthawuza kuti moyambirila mu nthawi, mndandanda, nambala,sitepe komanso kufunikila.
Mkhristu akuyenera kukachita zinthu zofunikila kwambiri moyambirila.
Chifukwa Chani Zinthu Zina Zikuyenera Kukachitidwa Moyambirila?
1. Chilichonse chimene sichidachitidwe moyambirila chimawonetsa kutsika kufunikila kwake.
Mulungu amadekha nafe. Ambiri sadamumvere Iye ndipo awonetsa kuti adangopitilila popanda vuto lili lonse. Kufunikila kwa Mawu a Mulungu kukuwonetsa ngati kukusiika pomwe tikupitililabe kuyenda m’kusamvera. Posakhalitsa icho chimene chimawoneka chofunikila kwambiri kuposa chili chonse chimasanduka chosafunikila ndi chosayenerela.
Lero, ndimatumikira pansi pa kudzoza ndipo ambiri amandilemekeza chifukwa cha utumiki. Koma ngati sindinamvere Mulungu pomwe ndinapanga, ndikanangokhala ngati dotolo chabe. Mkambilano wokhudzana ndi maitanidwe a Mulungu ukanaoneka ngati wosafunikira komanso wosayenera.
Kukhala pakati pa anzanga a zachipatala m’zipatala zosiyana siyana, lingaliro lakudzakhala m’busa likadakhala lonyozeka. Ndikadatha kunena kwa anzangawo, Tamverani ndikuuzeni lingaliro lopanda nzeru lomwe ndidali nalo. Kodi mukudziwa kuti ndinkafuna kudzakhala m’busa? Pamene ifeyo tidali achinyamata, tidali auzimu kwambiri komanso osatha kukhudzika.
Kodi mudayamba mutakunanapo ndi anthu achikulire omwe amanena kuti poyambilila adali pa mndandanda wa kukakhala ansembe? Mu ukalamba wawo, amayesera kukabwezeretsapo pa kusamvera kwawo kudzela mwa ana awo.
Ndikudziwa za munthu amene ankakakamiza mwana wake kukakhala wansembe.
Adanena kwa mwana wake wamwamuna, Mulungu adandiyitana kuti ndikakhale wansembe koma sindidachite motero. Iweyo ukhale wansembe ndipo ine ndidzakupatsa ndalama komasno katundu aliyense ndipo sudzasowa kanthu.
Kumapeto kwa moyo wawo amafuna atabwezeretsa pa umoyo wawo womwe adakhala wakusamvera ndi kusadziphatikiza kuchifuniro cha Mulungu.
Mzanga wokondedwa, nditha kukutsimikizila kuti pamene ukuchulukitsa mkayendedwe ka njira zako, malamulonso a Mulungu adzawoneka ngati akutali ndi wosafunikila. Chilipo chifukwa chake cha proton.
Proton, kapenanso kuti, kuchita zinthu zoyambirila moyambirila, amakupulumutsani inu ku chinyengo cha satana. Mulungu adzakusamalani ndipo adzakhala ndi inu pamene mukuyenda m’chifuniro chake.
2. China chili chonse chimene sichinachitidwe moyambirila chitha kusachitidwa
Kuchedwa nthawi zambiri kumatanthawuza kuchotsapo chinthucho. China chili chonse chomwe sichidachitidwe moyambilira chitha kusachitidwa. Sindinkadziwa kuti kuchedwetsa china chake kukhonza kudzetsa kuchotserapo chinthucho pa mndandanda wochita.
Padali tsiku limene ndidayenera kupanga ulendo kuchoka ku London kunka ku New York kukatumikila. Adandiyika pa mndandanda wokatumikila ku Maryland usiku umenewo. Mwatsoka, ndidali ndi manyamukidwe olawilila kwambiri a ndege kuchokera ku bwalo la ndege la Heathrow ku London, kunka ku Amsterdam ndiye kenako ndimayenera kukalumikiza kuchoka ku Amsterdam kuja kupita ku New York. Mwa mtundu wina wake sindidakhulupilire za nthawi yomwe ndidawona ya chiphaso changa cha ndege. Ndinkalingalira kuti nthawiyo idali yolawirila kwambiri kusiyana ndi m’mene imayenela kukhalila yolondola.
Pomwe ndidafika ku bwalo la ndegelo, kwa nthawi yoyamba m’moyo wanga, ndidali nditachedwa kwambiri kuti ndithe kukwera nawo ndegeyo. Ndidali ndita phonyana ndi nthawi ya kukwerela kwa pafupi fupi ma mphindi makumi awiri. Ndidakhumudwa. Ndidayenera kudikilila ndege ina yopita ku Amsterdam!
Simungathe kupanga ulendo wolumikiza kunka ku New York koma mutha kungo dikilila kunyamuka kotsatila,
adandiwuza. Ndidazindikila kuchokera kunthawiyo, kuti ndidali wakuthekera kukwanitsa kukafika ku New York ndi kwa nthawi yochepa chabe kukayenda pa galimoto kunka ku Maryland. Choncho ndidayimbila ku New York ndi kuwawuza abusawo za nthawi imene ndikadati ndikafikile kumeneko ndi kutinso tikafunikila kuyendetsedwa mwachangu kunka ku Maryland. Ndidamutsimikizila kuti tidali mu nthawi yabwino ndi kuti pologalamu ikakhalako posalabadila kuchedwa kwa pang’ono.
Ku Amsterdam, ndidakwera ndege yanga yakundilumikizitsa ku New York ndi chilimbikitso podziwa kuti adali akunyamuka posakhalitsa ndi kuti ndikhala ndili pa